NATHAN CHIKOYA lyrics : "Tidzakaonana - The Tribute"
[GEmCD]
This is a tribute to my dad and my brother John
Rest in peace.
[Verse 1]
Amai anga mutsalire ndiimfa ya amuna anu
Amai anga mutsalire ndiimfa ya mwana wanu.
Okufa MwaYesu alinawo moyo wina
Mtima ungasweke kulira mngalire koma chimodzi ndidziwa.
[Chorus]
Tidzakaonana futi Yesu pakubwera, Tidzakaonana futi Yesu pakubwera.
Tidzakaonana futi Yesu pakubwera, Tidzakaonana futi Yesu pakubwera.
[Verse 2]
Imfa iwe imfa ulibe chifundo Imfa iwe imfa watenga abale anga.
Ukutodola anthu umedza suukuta
Koma manyadzi kwaiwe Yesu akugonjetsa,
Koma manyadzi kwaiwe Yesu akugonjetsa.
[Verse 3]
Kukondwa komweko imfa kulibe,
Ndinyimbo yasopano tidzaimba kosaleka.
Alleluya, Alleluya, imfa wagonja, Alleluya, Alleluya, imfa wagonja.
Alleluya, Alleluya, imfa wagonja, Alleluya, Alleluya, imfa wagonja.
Submit Corrections